01/06/2026
Umboni oti alipo ndithu apolisi amene akugwira ntchito yawo mwa ukadaulo komanso molemekeza anthu amene akugwira nawo ntchito.
General akuti anawazepula akusekelera😆😆😆Anthu adzikhutira komanso kuyamikira m'mene apolisi awathandizira. Zimenezi ndi zimene ife kuno ku ICC tikulimbikitsa.
Inu munakumanapo nawo oterewa? Ulemu wanu apolisi amene muli a pfuko ili👍
01/06/2026
The weekend reminded us of an important lesson: not every result will go our way. While some are celebrating victories, others are still trying to come to terms with unexpected defeats. That’s the beauty of life; every setback and every triumph is an opportunity to learn, grow, and come back stronger.
Whether your plans worked out or not, today is a fresh chance to refocus, work hard, and keep moving forward.
Have a productive and positive week ahead!
30/05/2026
Madzulo ano mkulu wa ICC Commissioner Christopher Tukula akhala akufotokoza zambiri zokhudza bungweli mu pulogalamu ya Tisanthule Malamulo pa Mibawa Television. Onerani ndipo kudzera mu pulogalamu yi.
28/05/2026
From 23 to 27 June 2025, we conducted awareness-raising engagements with police officers in Blantyre, Mwanza, and Neno, aimed at sharing knowledge and experiences on how we can collectively promote public trust and confidence in the police service.
The feedback, questions, and contributions from the officers demonstrated the value and impact of these engagements as the Commission continues implementing its mandate of promoting rights-based policing.
26/05/2026
Did you know? The Malawi Police Act Schedule (Section 52) Code of disciplinary conduct for police officers (12) states that a police officer commits an offence against discipline who, without the knowledge and permission of the Inspector General, accepts directly or indirectly any gift, gratuity, present or reward from any member of the public in respect of anything done by him in the discharge of the duties of his office.
Akuti ndi kulakwira malamulo a ntchito ya polisi pamene wapolisi walandira mphatso kapena chothokoza, kaya chiongola dzanja, ena amati chiponda, kaya ya madzi, mwa njira ili yonse kuchokera kwa munthu aliyense chifukwa cha ntchito yomwe wapolisiyo wagwira popanda chiloleza kuchokera kwa mkulu wa polisi (Inspector General).
25/05/2026
Today, we celebrate ; a day that reminds us of our shared history, unity, resilience, and aspirations for a better future.
As we commemorate this important day, we recognize that access to justice is fundamental to peace, accountability, and development. A just society empowers citizens, protects the vulnerable, and strengthens democratic institutions.
Happy Africa Day!
21/05/2026
It’s quarter to Friday! Weekend plans are in the pipeline. Thursday has entered the chat like: “I’m not Friday, but you can already see Friday from here.” 😄
Arsenal fans this week are behaving like people who have just discovered happiness and free WiFi at the same time 😂🏆Kunonso tili nawo.
Now every small thing is a celebration:
“Good morning?” Champions.
“Pass the salt?” Champions.
“Weekend plans?” Parade route already confirmed 😄
As the celebrations continue, we would also like to remind everyone to celebrate responsibly and respect the law. Excessive excitement will not be accepted as a defense in a court of law. Akuti mungondimvetsetsa aaaa 😄😄😄 and unfortunately, police cells do not close for celebrations.
Koma ngati muli ndi dandaulo lokhudza apolisi, imbani mwa ulere ku 4314 ndipo mudzathandizidwa.
Happy Thursday!